Yohane 16:24 - Buku Lopatulika24 Kufikira tsopano simunapemphe kanthu m'dzina langa; pemphani, ndipo mudzalandira, kuti chimwemwe chanu chikwaniridwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Kufikira tsopano simunapempha kanthu m'dzina langa; pemphani, ndipo mudzalandira, kuti chimwemwe chanu chikwaniridwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Mpaka tsopano simunapemphe kanthu potchula dzina langa. Pemphani ndipo mudzalandira, kuti chimwemwe chanu chikhale chathunthu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Mpaka tsopano simunapemphe kalikonse mʼdzina langa. Pemphani ndipo mudzalandira, ndipo chimwemwe chanu chidzakhala chathunthu. Onani mutuwo |