Yohane 15:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo inunso muchita umboni, pakuti muli ndi Ine kuyambira chiyambi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo inunso muchita umboni, pakuti muli ndi Ine kuyambira chiyambi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Inunso mudzandichitira umboni, popeza kuti mwakhala nane kuyambira pa chiyambi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Inunso mudzandichitira umboni Ine, popeza mwakhala nane kuchokera pachiyambi.” Onani mutuwo |