Yohane 14:30 - Buku Lopatulika30 Sindidzalankhulanso zambiri ndi inu, pakuti mkulu wa dziko lapansi adza; ndipo alibe kanthu mwa Ine; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Sindidzalankhulanso zambiri ndi inu, pakuti mkulu wa dziko lapansi adza; ndipo alibe kanthu mwa Ine; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Sindilankhula nanunso zambiri tsopano ai, pakuti Satana, mfumu ya anthu ochimwa a dziko lapansi, alikudza. Iyeyo alibe mphamvu pa Ine, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Ine sindiyankhulanso nanu zambiri nthawi yayitali popeza wolamulira dziko lapansi akubwera. Iye alibe mphamvu pa Ine, Onani mutuwo |