Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 14:29 - Buku Lopatulika

29 Ndipo tsopano ndakuuzani chisanachitike, kuti pamene chitachitika mukakhulupirire.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ndipo tsopano ndakuuzani chisanachitike, kuti pamene chitachitika mukakhulupirire.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Ndakuuziranitu zimenezi tsopano zisanachitike, kuti zikadzachitika, mudzakhulupirire.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Ine ndakuwuzani tsopano zisanachitike, kuti zikadzachitika mudzakhulupirire.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 14:29
4 Mawu Ofanana  

Kuyambira tsopano ndinena kwa inu, chisadachitike, kuti pamene chitachitika, mukakhulupirire kuti ndine amene.


Sindidzalankhulanso zambiri ndi inu, pakuti mkulu wa dziko lapansi adza; ndipo alibe kanthu mwa Ine;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa