Yohane 14:25 - Buku Lopatulika25 Izi ndalankhula nanu, pakukhala ndi inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Izi ndalankhula nanu, pakukhala ndi inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 “Zimenezi ndakuuzani ndikadali nanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 “Ndayankhula zonsezi ndikanali nanu. Onani mutuwo |