Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 14:25 - Buku Lopatulika

25 Izi ndalankhula nanu, pakukhala ndi inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Izi ndalankhula nanu, pakukhala ndi inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 “Zimenezi ndakuuzani ndikadali nanu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 “Ndayankhula zonsezi ndikanali nanu.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 14:25
8 Mawu Ofanana  

Kuyambira tsopano ndinena kwa inu, chisadachitike, kuti pamene chitachitika, mukakhulupirire kuti ndine amene.


Wosandikonda Ine sasunga mau anga; ndipo mau amene mumva sali mau anga, koma a Atate wondituma Ine.


Koma Nkhosweyo, Mzimu Woyera, amene Atate adzamtuma m'dzina langa, Iyeyo adzaphunzitsa inu zonse, nadzakumbutsa inu zinthu zonse zimene ndinanena kwa inu.


Ndipo tsopano ndakuuzani chisanachitike, kuti pamene chitachitika mukakhulupirire.


Izi ndalankhula ndi inu, kuti chimwemwe changa chikhale mwa inu, ndi kuti chimwemwe chanu chidzale.


Ndili nazo zambirinso zakunena kwa inu, koma simungathe kuzisenza tsopano lino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa