Yohane 14:20 - Buku Lopatulika20 Tsiku lomwelo mudzazindikira kuti ndili Ine mwa Atate wanga, ndi inu mwa Ine, ndi Ine mwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Tsiku lomwelo mudzazindikira kuti ndili Ine mwa Atate wanga, ndi inu mwa Ine, ndi Ine mwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Tsiku limenelo mudzadziŵa kuti Ine ndimakhala mwa Atate, ndipo inu mumakhala mwa Ine, monga Ine ndimakhala mwa inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Tsiku limenelo inu mudzazindikira kuti Ine ndili mwa Atate, ndipo inu muli mwa Ine, ndipo Ine ndili mwa inu. Onani mutuwo |