Yohane 14:14 - Buku Lopatulika14 Ngati mudzapempha kanthu m'dzina langa, ndidzachita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ngati mudzapempha kanthu m'dzina langa, ndidzachita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ngati mudzandipempha kanthu potchula dzina langa ndidzakachitadi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ngati mudzapempha kanthu kalikonse mʼdzina langa, Ine ndidzachita. Onani mutuwo |