Yohane 14:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo chimene chilichonse mukafunse m'dzina langa, ndidzachichita, kuti Atate akalemekezedwe mwa Mwana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo chimene chilichonse mukafunse m'dzina langa, ndidzachichita, kuti Atate akalemekezedwe mwa Mwana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Chilichonse chomwe mudzachipemphe potchula dzina langa ndidzachita, kuti Atate adzalemekezedwe mwa Mwana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndipo Ine ndidzachita chilichonse chimene inu mudzapempha mʼdzina langa kuti Atate alemekezedwe mwa Mwana. Onani mutuwo |