Yohane 13:35 - Buku Lopatulika35 Mwa ichi adzazindikira onse kuti muli ophunzira anga, ngati muli nacho chikondano wina ndi mnzake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Mwa ichi adzazindikira onse kuti muli ophunzira anga, ngati muli nacho chikondano wina ndi mnzake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Mukamakondana, anthu onse adzadziŵa kuti ndinudi ophunzira anga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Mukamakondana aliyense adzadziwa kuti ndinu ophunzira anga.” Onani mutuwo |