Yohane 12:46 - Buku Lopatulika46 Ndadza Ine kuunika kudziko lapansi, kuti yense wokhulupirira Ine asakhale mumdima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Ndadza Ine kuunika kudziko lapansi, kuti yense wokhulupirira Ine asakhale mumdima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Ine ndine kuŵala, ndipo ndidadza pansi pano, kuti munthu aliyense wokhulupirira Ine, asamayende mu mdima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Ine ndabwera mʼdziko lapansi monga kuwunika, kotero palibe amene amakhulupirira Ine nʼkumakhalabe mu mdima. Onani mutuwo |