Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 12:45 - Buku Lopatulika

45 Ndipo wondiona Ine aona amene anandituma Ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

45 Ndipo wondiona Ine aona amene anandituma Ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

45 Ndipo munthu woona Ine, amaonanso Iye amene adandituma.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

45 Iye amene waona Ine, waonanso Iye amene anandituma Ine.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 12:45
8 Mawu Ofanana  

Izi anati Yesaya, chifukwa anaona ulemerero wake; nalankhula za Iye.


Sindikadachita mwa iwo ntchito zosachita wina, sakadakhala nalo tchimo; koma tsopano anaona, nada Ine ndi Atate wanganso.


Pakuti chifuniro cha Atate wanga ndi ichi, kuti yense wakuyang'ana Mwana, ndi kukhulupirira Iye, akhale nao moyo wosatha; ndipo Ine ndidzamuukitsa iye tsiku lomaliza.


Pakuti Mulungu amene anati, Kuunika kudzawala kutuluka mumdima, ndiye amene anawala m'mitima yathu kutipatsa chiwalitsiro cha chidziwitso cha ulemerero wa Mulungu pankhope pa Yesu Khristu.


amene ali fanizo la Mulungu wosaonekayo, wobadwa woyamba wa chilengedwe chonse;


ameneyo, pokhala ali chinyezimiro cha ulemerero wake, ndi chizindikiro chenicheni cha chikhalidwe chake, nanyamula zonse ndi mau a mphamvu yake, m'mene adachita chiyeretso cha zoipa, anakhala padzanja lamanja la Ukulu mu Mwamba,


Ndipo tidziwa kuti Mwana wa Mulungu wafika, natipatsa ife chidziwitso, kuti tizindikire Woonayo, ndipo tili mwa Woonayo, mwa Mwana wake Yesu Khristu. Iye ndiye Mulungu woona ndi moyo wosatha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa