Yohane 12:42 - Buku Lopatulika42 Kungakhale kotero, ambiri a mwa akulu anakhulupirira Iye; koma chifukwa cha Afarisi sanavomereze, kuti angaletsedwe m'sunagoge, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Kungakhale kotero, ambiri a mwa akulu anakhulupirira Iye; koma chifukwa cha Afarisi sanavomereza, kuti angaletsedwe m'sunagoge, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Komabe ambiri mwa atsogoleri ao omwe adakhulupirira Yesu. Koma chifukwa cha Afarisi iwo sankanena zimenezo poyera. Ankaopa kuti angaŵadule ku mpingo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Komabe pa nthawi yomweyi ambiri ngakhale atsogoleri anakhulupirira Iye. Koma chifukwa cha Afarisi iwo sanavomereze chikhulupiriro chawo chifukwa amaopa kuti angawatulutse mʼsunagoge; Onani mutuwo |