Yohane 12:38 - Buku Lopatulika38 kuti mau a Yesaya mneneri akakwaniridwe, amene anati, Ambuye, wakhulupirira ndani kulalikira kwathu? Ndipo mkono wa Ambuye wavumbulutsidwa kwa yani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 kuti mau a Yesaya mneneri akakwaniridwe, amene anati, Ambuye, wakhulupirira ndani kulalikira kwathu? Ndipo mkono wa Ambuye wavumbulutsidwa kwa yani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Zidaatero kuti zipherezere zimene mneneri Yesaya adaaneneratu kuti, “Ambuye, ndani wakhulupirira kulalika kwathu? Ndani wazindikira mphamvu za Ambuye pa zimenezi?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Izi zinakwaniritsa mawu a mneneri Yesaya kuti: “Ambuye, wakhulupirira uthenga wathu ndani, ndipo ndi kwa yani komwe mkono wa Ambuye wavumbulutsidwa?” Onani mutuwo |