Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 12:37 - Buku Lopatulika

37 Koma angakhale adachita zizindikiro zambiri zotere pamaso pao iwo sanakhulupirire Iye;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Koma angakhale adachita zizindikiro zambiri zotere pamaso pao iwo sanakhulupirira Iye;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Ngakhale Yesu adaachita zozizwitsa zambiri chotere pamaso pao, komabe iwo sadamkhulupirire.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Ngakhale Yesu anachita zizindikiro zodabwitsa zonsezi pamaso pawo, sanamukhulupirirebe.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 12:37
9 Mawu Ofanana  

Pomwepo Iye anayamba kutonza mizindayo, m'mene zinachitidwa zambiri za ntchito zamphamvu zake, chifukwa kuti siinatembenuke.


Koma anati kwa iye, Ngati samvera Mose ndi aneneri, sadzakopeka mtima ngakhale wina akauka kwa akufa.


Anadza kwa zake za Iye yekha, ndipo ake a mwini yekha sanamlandire Iye.


Koma ndadziwa Ine kuti mumandimva Ine nthawi zonse; koma chifukwa cha khamu la anthu alikuimirira pozungulira ndinanena ichi, kuti akhulupirire kuti Inu munandituma Ine.


Pokhala muli nako kuunika, khulupirirani kuunikako, kuti mukakhale ana a kuunikako. Izi Yesu analankhula, nachoka nawabisalira.


kuti mau a Yesaya mneneri akakwaniridwe, amene anati, Ambuye, wakhulupirira ndani kulalikira kwathu? Ndipo mkono wa Ambuye wavumbulutsidwa kwa yani?


Sindikadachita mwa iwo ntchito zosachita wina, sakadakhala nalo tchimo; koma tsopano anaona, nada Ine ndi Atate wanganso.


Chiyambi ichi cha zizindikiro zake Yesu anachita mu Kana wa mu Galileya naonetsera ulemerero wake; ndipo ophunzira ake anakhulupirira Iye.


Ndipo khamu lalikulu la anthu linamtsata Iye, chifukwa anaona zizindikiro zimene anachita pa odwala.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa