Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 12:33 - Buku Lopatulika

33 Koma ananena ichi ndi kuzindikiritsa imfa yanji akuti adzafa nayo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Koma ananena ichi ndi kuzindikiritsa imfa yanji akuti adzafa nayo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 (Adaanena mau ameneŵa kuti aŵadziŵitse za m'mene analikudzafera.)

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Iye ananena izi kuti aonetse mmene adzafere.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 12:33
2 Mawu Ofanana  

kuti mau a Yesu akwaniridwe, amene ananena akuzindikiritsa imfa imene akuti adzafa nayo.


Koma ichi ananena ndi kuzindikiritsa imfa imene adzalemekeza nayo Mulungu. Ndipo m'mene ananena ichi, anati kwa iye, Nditsate Ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa