Yohane 11:38 - Buku Lopatulika38 Pamenepo Yesu, ndi kudzumanso mwa Iye yekha anadza kumanda. Koma panali phanga, ndipo mwala unaikidwa pamenepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Pamenepo Yesu, ndi kudzumanso mwa Iye yekha anadza kumanda. Koma panali phanga, ndipo mwala unaikidwa pamenepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Yesu adavutikanso mu mtima, nakafika ku manda amene anali phanga. Pakhomo pake panali chimwala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Yesu atakhudzidwanso kwambiri anafika ku manda. Manda akewo anali phanga ndipo anatsekapo ndi mwala. Onani mutuwo |