Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 10:37 - Buku Lopatulika

37 Ngati sindichita ntchito za Atate wanga, musakhulupirira Ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Ngati sindichita ntchito za Atate wanga, musakhulupirira Ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Ngati sindichita ntchito zimene Atate anga adandipatsa, musandikhulupirire.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Musandikhulupirire Ine ngati sindichita ntchito za Atate anga.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 10:37
7 Mawu Ofanana  

Yesu anayankha iwo, Ndakuuzani, ndipo simukhulupirira. Ntchitozi ndidzichita Ine m'dzina la Atate wanga, zimenezi zindichitira umboni.


Yesu anayankha iwo, Ndakuonetsani inu ntchito zabwino zambiri za kwa Atate; chifukwa cha ntchito yiti ya izo mundiponya miyala?


Sukhulupirira kodi kuti ndili Ine mwa Atate, ndi Atate ali mwa Ine? Mau amene ndinena Ine kwa inu sindilankhula kwa Ine ndekha; koma Atate wokhala mwa Ine achita ntchito zake.


Sindikadachita mwa iwo ntchito zosachita wina, sakadakhala nalo tchimo; koma tsopano anaona, nada Ine ndi Atate wanganso.


Ngati ndichita umboni wa Ine ndekha, umboni wanga suli woona.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa