Yohane 10:37 - Buku Lopatulika37 Ngati sindichita ntchito za Atate wanga, musakhulupirira Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ngati sindichita ntchito za Atate wanga, musakhulupirira Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Ngati sindichita ntchito zimene Atate anga adandipatsa, musandikhulupirire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Musandikhulupirire Ine ngati sindichita ntchito za Atate anga. Onani mutuwo |