Yohane 10:29 - Buku Lopatulika29 Atate wanga, amene anandipatsa izo, ali wamkulu ndi onse; ndipo palibe wina ngathe kuzikwatula m'dzanja la Atate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Atate wanga, amene anandipatsa izo, ali wamkulu ndi onse; ndipo palibe wina ngathe kuzikwatula m'dzanja la Atate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Atate anga amene adandipatsa nkhosazo amapambana onse, ndipo palibe amene angathe kuzilanda m'manja mwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Atate anga, amene anandipatsa Ine, ndi akulu kuposa onse. Palibe amene angazikwatule mʼdzanja la Atate anga. Onani mutuwo |