Yohane 1:35 - Buku Lopatulika35 M'mawa mwakenso analikuimirira Yohane ndi awiri a ophunzira ake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 M'mawa mwakenso analikuimirira Yohane ndi awiri a ophunzira ake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 M'maŵa mwakenso Yohane anali pamalo pomwepo pamodzi ndi ophunzira ake ena aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Pa tsiku lotsatira Yohane analinso pamenepo pamodzi ndi awiri a ophunzira ake. Onani mutuwo |