Yobu 9:2 - Buku Lopatulika2 Zoona, ndidziwa kuti chili chotero. Koma munthu adzakhala wolungama bwanji kwa Mulungu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Zoona, ndidziwa kuti chili chotero. Koma munthu adzakhala wolungama bwanji kwa Mulungu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Inde, ndikudziŵa kuti zimenezi ndi zoona, koma nanga munthu angathe bwanji kukhala wolungama pamaso pa Mulungu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Zoonadi, ndikudziwa kuti zimenezi ndi zoona. Koma munthu angathe bwanji kukhala wolungama pamaso pa Mulungu? Onani mutuwo |