Yobu 8:4 - Buku Lopatulika4 Chinkana ana ako anamchimwira Iye, ndipo anawapereka mwa kulakwa kwao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Chinkana ana ako anamchimwira Iye, ndipo anawapereka mwa kulakwa kwao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Kapena ana ako adamchimwira, nkuwona Mulungu adaŵalanga chifukwa cha zochimwa zaozo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pamene ana ako anamuchimwira Mulungu, Iye anawapereka kuti alangidwe chifukwa cha tchimo lawo. Onani mutuwo |