Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 8:1 - Buku Lopatulika

1 Pamenepo anayankha Bilidadi Msuki, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Pamenepo anayankha Bilidadi Msuki, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Apo Bilidadi, Msuhi, adayankha Yobe kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Pamenepo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yobu 8:1
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo Bilidadi wa ku Suki anayankha, nati,


Atamva tsono mabwenzi atatu a Yobu za choipa ichi chonse chidamgwera, anadza, yense kuchokera kwao, Elifazi wa ku Temani, ndi Bilidadi Msuki, ndi Zofari wa ku Naama, napangana kudzafika kumlirira ndi kumsangalatsa.


Pamenepo Bilidadi wa ku Suki anayankha, nati,


Mulekeranji kukhululukira kulakwa kwanga ndi kundichotsera mphulupulu yanga? Popeza tsopano ndidzagona kufumbi; mudzandifunafuna, koma ine palibe.


Udzanena izi kufikira liti? Ndipo mau a pakamwa pako adzakhala ngati namondwe kufikira liti?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa