Yobu 7:9 - Buku Lopatulika9 Mtambo wapita watha, momwemo wakutsikira kumanda sadzakwerakonso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Mtambo wapita watha, momwemo wakutsikira kumanda sadzakwerakonso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu woloŵa ku manda sabwerako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. Onani mutuwo |