Yobu 7:8 - Buku Lopatulika8 Diso la amene andiona silidzandionanso, maso ako adzandipenyetsetsa, koma ine palibe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Diso la amene andiona silidzandionanso, maso ako adzandipenyetsetsa, koma ine palibe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Amene akundiwona tsopano, sadzandiwonanso. Nthaŵi yomwe iye adzandifunafuna, ine ndidzakhala nditapita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Amene akundiona tsopano akundiona; mudzandifunafuna koma sindidzapezekanso. Onani mutuwo |