Yobu 7:7 - Buku Lopatulika7 Kumbukira kuti moyo wanga ndiwo mphepo, diso langa silidzaonanso chokoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Kumbukira kuti moyo wanga ndiwo mphepo, diso langa silidzaonanso chokoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Inu Mulungu kumbukirani kuti moyo wanga uli ngati mpweya. Masiku abwino sindidzaŵaonanso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Inu Mulungu kumbukirani kuti moyo wanga uli ngati mpweya; sindidzaonanso masiku achisangalalo. Onani mutuwo |