Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 7:2 - Buku Lopatulika

2 Monga kapolo woliralira mthunzi, monga wolembedwa ntchito ayembekezera mphotho yake,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Monga kapolo woliralira mthunzi, monga wolembedwa ntchito ayembekezera mphotho yake,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Paja kapolo amalakalaka mthunzi, wantchito amayembekezera malipiro ake,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Monga ngati kapolo wolakalaka mthunzi wa nthawi yamadzulo, kapena ngati munthu waganyu woyembekezera malipiro ake,

Onani mutuwo Koperani




Yobu 7:2
11 Mawu Ofanana  

Ndipo Hamori ananena ndi iwo, kuti, Mtima wa Sekemu mwana wanga umkhumba mwana wako wamkazi: umpatsetu kuti akhale mkazi wake.


Kodi munthu alibe nkhondo kunja kuno? Kodi masiku ake sakunga masiku a wolembedwa ntchito?


momwemo anandilowetsa miyezi yopanda pake. Nandiikiratu zowawa usiku ndi usiku.


Ndinatsegula pakamwa panga, ndi kupuma wefuwefu; popeza ndinakhumba malamulo anu.


Nditambalitsira manja anga kwa Inu: Moyo wanga ulira Inu monga dziko lolira mvula.


Lalikirani nkhondo yakumenyana ndi iye; ukani, tikwere pakati pa usana. Tsoka kwa ife! Pakuti dzuwa lapendeka, mithunzi ya madzulo yatambasuka.


Usamasautsa mnansi wako, kapena kulanda zake; mphotho yake ya wolipidwa isakhale ndi iwe kufikira m'mawa.


Ndipo Yehova Mulungu anaikiratu msatsi, naumeretsera Yona, uchite mthunzi pamutu pake, kumlanditsa m'nsautso yake. Ndipo Yona anakondwera kwambiri chifukwa cha msatsiwo.


Ndipo ndidzayandikiza kwa inu kuti ndiweruze; ndipo ndidzakhala mboni yakufulumira kutsutsa obwebweta, ndi achigololo, ndi olumbira monama; ndi iwo akunyenga wolembedwa ntchito pa kulipira kwake, akazi amasiye, ndi ana amasiye, ndi wakuipsa mlandu wa mlendo, osandiopa Ine, ati Yehova wa makamu.


Pa tsiku lake muzimpatsa kulipira kwake, lisalowepo dzuwa; pakuti ndiye waumphawi, ndi mtima wake ukhumba uku; kuti angakulirireni kwa Yehova, ndipo kukukhalireni tchimo.


Taonani, mphotho ya antchitowo anasenga m'minda yanu, yosungidwa ndi inu powanyenga, ifuula; ndipo mafuulo a osengawo adalowa m'makutu a Ambuye wa makamu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa