Yobu 7:2 - Buku Lopatulika2 Monga kapolo woliralira mthunzi, monga wolembedwa ntchito ayembekezera mphotho yake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Monga kapolo woliralira mthunzi, monga wolembedwa ntchito ayembekezera mphotho yake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Paja kapolo amalakalaka mthunzi, wantchito amayembekezera malipiro ake, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Monga ngati kapolo wolakalaka mthunzi wa nthawi yamadzulo, kapena ngati munthu waganyu woyembekezera malipiro ake, Onani mutuwo |