Yobu 7:1 - Buku Lopatulika1 Kodi munthu alibe nkhondo kunja kuno? Kodi masiku ake sakunga masiku a wolembedwa ntchito? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Kodi munthu alibe nkhondo kunja kuno? Kodi masiku ake sakunga masiku a wolembedwa ntchito? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 “Moyo wa munthu pa dziko lapansi ndi wa ntchito yakalavulagaga. Masiku ake ali ngati a munthu waganyu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Kodi munthu sakhala ndi ntchito yowawa pa dziko lapansi? Kodi masiku ake sali ngati munthu waganyu? Onani mutuwo |