Yobu 6:9 - Buku Lopatulika9 Chimkomere Mulungu kundiphwanya, alole dzanja lake lindilikhe! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Chimkomere Mulungu kundiphwanya, alole dzanja lake lindilikhe! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Achikhala kudaamkomera Mulungu kuti anditswanye, achikhala adaandimenya ndi dzanja lake, nkundiwonongeratu! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 achikhala chinamukomera Mulungu kuti anditswanye, kulola dzanja lake kuti lindimenye ndi kundiwonongeratu! Onani mutuwo |