Yobu 6:8 - Buku Lopatulika8 Ha! Ndikadakhala nacho chimene ndichipempha, Mulungu akadandipatsa chimene ndichilira! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ha! Ndikadakhala nacho chimene ndichipempha, Mulungu akadandipatsa chimene ndichilira! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 “Achikhala ndidaalandira chomwe ndikufuna, achikhala Mulungu adaandipatsa chimene ndikukhumba! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Aa, ndikanalandira chimene ndikuchipempha, chikhala Mulungu anandipatsa chimene ndikuchiyembekezera, Onani mutuwo |