Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 6:3 - Buku Lopatulika

3 Pakuti zikadalemera tsopano koposa mchenga wa kunyanja; chifukwa chake mau anga ndasonthokera kunena.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Pakuti zikadalemera tsopano koposa mchenga wa kunyanja; chifukwa chake mau anga ndasonthokera kunena.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 bwenzi atalemera kupambana mchenga wonse wam'nyanja. Nchifukwa chake kulankhula kwanga kuli kokadzulira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Ndithu, zikanalemera kupambana mchenga wa ku nyanja; nʼchifukwa chake mawu anga akhala okhadzula.

Onani mutuwo Koperani




Yobu 6:3
7 Mawu Ofanana  

Lero lomwe kudandaula kwanga kumawawa; kulanga kwanga kuposa kubuula kwanga m'kulemera kwake.


andiyese ndi muyeso wolingana, kuti Mulungu adziwe ungwiro wanga.


Inu, Yehova, Mulungu wanga, zodabwitsa zanu mudazichita nzambiri, ndipo zolingirira zanu za pa ife; palibe wina wozifotokozera Inu; ndikazisimba ndi kuzitchula, zindichulukira kuziwerenga.


Mundikhalitsa maso; ndigwidwa mtima wosanena kanthu.


Mwala ulemera, mchenga ndiwo katundu; koma mkwiyo wa chitsiru upambana kulemera kwake.


Idzani kuno kwa Ine nonsenu akulema ndi kuthodwa, ndipo Ine ndidzakupumulitsani inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa