Yobu 6:2 - Buku Lopatulika2 Mwenzi atayesa bwino chisoni changa, ndi kuika matsoka anga pamodzi pamuyeso! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mwenzi atayesa bwino chisoni changa, ndi kuika matsoka anga pamodzi pamuyeso! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Achikhala mavuto anga adaayesedwa, achikhala masoka anga adaaŵaika pa sikelo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Achikhala mavuto anga anayezedwa, ndipo zipsinjo zanga zonse zikanayikidwa pa sikelo! Onani mutuwo |