Yobu 5:3 - Buku Lopatulika3 Ndinapenya wopusa woyala mizu; koma pomwepo ndinatemberera pokhala pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndinapenya wopusa woyala mizu; koma pomwepo ndinatemberera pokhala pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ine ndidaona chitsiru chitamera mizu, koma mwadzidzidzi nyumba yake ndidaitemberera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ine ndinaona chitsiru chitamera mizu, koma mwadzidzidzi nyumba yake inatembereredwa. Onani mutuwo |