Yobu 5:2 - Buku Lopatulika2 Pakuti mkwiyo umapha wopusa, ndi nsanje imakantha wopanda pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pakuti mkwiyo umapha wopusa, ndi nsanje imakantha wopanda pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pajatu mkwiyo umapha chitsiru, ndipo njiru zimaononga wopusa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mkwiyo umapha chitsiru, ndipo njiru imawononga wopusa. Onani mutuwo |