Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 5:2 - Buku Lopatulika

2 Pakuti mkwiyo umapha wopusa, ndi nsanje imakantha wopanda pake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Pakuti mkwiyo umapha wopusa, ndi nsanje imakantha wopanda pake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Pajatu mkwiyo umapha chitsiru, ndipo njiru zimaononga wopusa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Mkwiyo umapha chitsiru, ndipo njiru imawononga wopusa.

Onani mutuwo Koperani




Yobu 5:2
19 Mawu Ofanana  

Pamene Rakele anaona kuti sanambalire Yakobo ana, Rakele anamchitira mkulu wake nsanje; nati kwa Yakobo, Ndipatse ana ndingafe.


Ndipo Onani anadziwa kuti mbeu siidzakhala yake: ndipo panali pamene iye analowana naye mkazi wa mbale wake, kuti anaitaya pansi, kuti angampatse mbeu kwa mkulu wake.


Iwe wodzing'amba mumkwiyo mwako, kodi dziko lapansi lisiyidwe chifukwa cha iwe? Kapena thanthwe lisunthike m'malo mwake?


Anthu opusa azunzika chifukwa cha zolakwa zao, ndi chifukwa cha mphulupulu zao.


Wauchitsiru amati mumtima mwake, Kulibe Mulungu. Achita zovunda, achita ntchito zonyansa; kulibe wakuchita bwino.


Ndinati kwa odzitamandira, musamachita zodzitamandira; ndi kwa oipa, Musamakweza nyanga;


Munthu wopulukira sachidziwa; ndi munthu wopusa sachizindikira ichi;


Mkwiyo wa chitsiru udziwika posachedwa; koma wanzeru amabisa manyazi.


Wosunga lamulo asunga moyo wake; wonyalanyaza mayendedwe ake adzafa.


Munthu waukali alipire mwini; pakuti ukampulumutsa udzateronso.


Mwala ulemera, mchenga ndiwo katundu; koma mkwiyo wa chitsiru upambana kulemera kwake.


Achibwana inu, chenjerani, opusa inu, khalani ndi mtima wozindikira;


Usakangaze mumtima mwako kukwiya; pakuti mkwiyo ugona m'chifuwa cha zitsiru.


Ndipo Efuremu ali ngati nkhunda yopusa yopanda nzeru; aitanira kwa Ejipito, amuka kwa Asiriya.


Ndipo Mulungu anati kwa Yona, Uyenera kodi kupsa mtima chifukwa cha msatsiwo? Nati iye, Ee, kundiyenera ine kupsa mtima mpaka imfa.


koma kwa iwo andeu, ndi osamvera choonadi, koma amvera chosalungama, adzabwezera mkwiyo ndi kuzaza,


Pakuti mwa iwo akhala akukwawira m'nyumba, nagwira akazi opusa, osenza akatundu a zoipa zao, otengedwa nazo zilakolako za mitundumitundu:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa