Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 5:1 - Buku Lopatulika

1 Itana tsono; pali wina wakukuyankha kodi? Ndipo udzatembenukira kwa yani wa oyera mtimawo?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Itana tsono; pali wina wakukuyankha kodi? Ndipo udzatembenukira kwa yani wa oyera mtimawo?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 “Iwe Yobe, itana tsono. Kodi alipo wina aliyense adzakuyankhe? Kodi ndi kwa mngelo uti ungapeze thandizo?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 “Itana ngati ungathe, koma ndani adzakuyankhe? Kodi ndi kwa mngelo uti ungapezeko thandizo?

Onani mutuwo Koperani




Yobu 5:1
12 Mawu Ofanana  

Taona, Mulungu sakhulupirira opatulika ake; ngakhale m'mwamba simuyera pamaso pake.


Mupatse chigwiriro tsono, mundikhalire chikole Inu nokha kwanu; ndani adzapangana nane kundilipirira?


Taona, sakhulupirira atumiki ake; nawanenera amithenga ake zopusa;


Ndipo kumisasa anachita nao nsanje Mose ndi Aroni woyerayo wa Yehova.


Za oyera mtima okhala padziko lapansi, iwo ndiwo omveka mbiri, mwa iwowo muli chikondwero changa chonse.


Ndipo kumwamba kudzalemekeza zodabwitsa zanu, Yehova; chikhulupiriko chanunso mu msonkhano wa oyera mtima.


Khalani chete pamaso pa Ine, zisumbu inu, anthu atengenso mphamvu; ayandikire; pamenepo alankhule; tiyeni tiyandikire pamodzi kuchiweruziro.


Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu, mwa chifuniro cha Mulungu, kwa oyera mtima amene ali mu Efeso, ndi kwa iwo okhulupirika mwa Khristu Yesu:


Chifukwa chake ifenso, popeza tizingidwa nao mtambo waukulu wotere wa mboni, titaye cholemetsa chilichonse, ndi tchimoli limangotizinga, ndipo tithamange mwachipiriro makaniwo adatiikira, ndi kupenyerera woyambira ndi womaliza wa chikhulupiriro chathu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa