Yobu 41:2 - Buku Lopatulika2 Kodi ukhoza kumanga m'mphuno ndi mlulu? Kapena kuboola nsagwada wake ndi mbedza? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Kodi ukhoza kumanga m'mphuno ndi mlulu? Kapena kuboola nsagwada wake ndi mbedza? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kodi ungathe kuchimanga chingwe m'mphuno mwake, kapena kuchiboola nsagwada ndi mbedza? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Kodi ungathe kumanga chingwe mʼmphuno mwake, kapena kubowola nsagwada zake ndi mbedza? Onani mutuwo |