Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 41:1 - Buku Lopatulika

1 Kodi ukhoza kukoka Leviyatani ndi mbedza? Kapena kukanikiza kalandira wake ndi chingwe?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Kodi ukhoza kukoka Leviyatani ndi mbedza? Kapena kukanikiza kalandira wake ndi chingwe?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Kodi ungathe kuchikoka ndi mbedza ya nsomba chilombo chija cha Leviyatani, kapena kukanikiza lilime lake pansi ndi chingwe?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 “Kodi ungathe kukoka ngʼona ndi mbedza ya nsomba kapena kukanikiza lilime lake pansi ndi chingwe?

Onani mutuwo Koperani




Yobu 41:1
6 Mawu Ofanana  

ndi zamoyo zonse zili pamodzi ndi inu, zouluka, ng'ombe, ndi zinyama zonse za dziko lapansi, pamodzi ndi inu; zonse zotuluka m'chingalawa, zinyama zonse za dziko lapansi.


Autemberere iwo akutemberera usana, Odziwa kuutsa Leviyatani.


Ikakhala maso, munthu adzaigwira kodi? Kapena kuboola m'mphuno mwake ili m'khwekhwe?


M'mwemo muyenda zombo; ndi Leviyatani amene munamlenga aseweremo.


Mudaphwanya mitu ya Leviyatani; mudampereka akhale chakudya cha zilombo za m'chipululu.


Tsiku limenelo Yehova ndi lupanga lake lolimba ndi lalikulu ndi lamphamvu adzalanga Leviyatani njoka yothamanga, ndi Leviyatani njoka yopindikapindika; nadzapha ching'ona chimene chili m'nyanja.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa