Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 40:3 - Buku Lopatulika

3 Pamenepo Yobu anayankha Yehova nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Pamenepo Yobu anayankha Yehova nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Apo Yobe adayankha Chauta kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Pamenepo Yobu anayankha Yehova:

Onani mutuwo Koperani




Yobu 40:3
8 Mawu Ofanana  

Nalankhula Yobu nati,


Pakuti pali wina kodi anati kwa Mulungu, ndasenza kulanga kwanu, ndingakhale sindinalakwe?


Kodi wodzudzulayo atsutsane ndi Wamphamvuyonse? Wochita makani ndi Mulungu ayankhe.


Taonani, ndakhululuka ine, ndidzakubwezerani mau otani? Ndigwira pakamwa.


Pamenepo Yobu anayankha Yehova, nati,


chifukwa chake ndekha ndidzinyansa, ndi kulapa m'fumbi ndi mapulusa.


Kunali tsono atanena Yehova mau awa kwa Yobu, Yehova anati kwa Elifazi wa ku Temani, Mkwiyo wanga wakuyakira iwe ndi mabwenzi ako awiri, pakuti simunandinenere choyenera monga ananena mtumiki wanga Yobu.


Potero mverani Mulungu; koma kanizani mdierekezi, ndipo adzakuthawani inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa