Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 4:9 - Buku Lopatulika

9 Atayika ndi mpweya wa Mulungu, nathedwa ndi mpumo wa mkwiyo wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Atayika ndi mpweya wa Mulungu, nathedwa ndi mpumo wa mkwiyo wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Monga momwe mphepo ya mkuntho imasakazira zinthu, Mulungu amaŵaononga ndi mkwiyo wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Iwo amaphedwa ndi mpweya wa Mulungu; amawonongeka ndi mpweya waukali wa mkwiyo wake.

Onani mutuwo Koperani




Yobu 4:9
13 Mawu Ofanana  

Taonani, ndidzalonga mwa iye mzimu wakuti adzamva mbiri, nadzabwerera kunka ku dziko lake, ndipo ndidzamgwetsa ndi lupanga m'dziko lake.


ndipo taonani, inadza mphepo yaikulu yochokera kuchipululu, niomba pangodya zonse zinai za nyumbayo, nigwa pa anyamatawo, nafa; ndipo ndapulumuka ine ndekha kudzakuuzani.


Sadzachoka mumdima; lawi la moto lidzaumitsa nthambi zake; ndipo adzachoka ndi mpumo wa m'kamwa mwake.


Tsanulira mkwiyo wako wosefuka, nupenyerere aliyense wodzikuza ndi kumchepetsa.


Uwakwirire pamodzi m'fumbi, uzimange nkhope zao pobisika.


Ndipo zidaoneka zoyendamo madzi, nafukuka maziko a dziko lapansi, mwa kudzudzula kwanu, Yehova, mwa mpumo wa mpweya wa m'mphuno mwanu.


Munaombetsa mphepo yanu, nyanja inawamiza; anamira m'madzi aakulu ngati mtovu.


Ndipo ndi mpumo wa m'mphuno mwanu madzi anaunjikika, mayendedwe ake anakhala chilili ngati mulu; zozama zinalimba m'kati mwa nyanja.


koma ndi chilungamo adzaweruza aumphawi, nadzadzudzulira ofatsa a m'dziko moongoka; ndipo adzamenya dziko lapansi ndi chibonga cha kukamwa kwake, nadzapha oipa ndi mpweya wa milomo yake.


Pakuti Tofeti wakonzedwa kale, inde chifukwa cha mfumu wakonzedweratu; Iye wazamitsapo, nakuzapo; mulu wakewo ndi moto ndi nkhuni zambiri; mpweya wa Yehova uuyatsa ngati mtsinje wa sulufure.


udzu unyala, duwa lifota; chifukwa mpweya wa Yehova waombapo; zoonadi anthu ndi udzu.


Ndipo pamenepo adzavumbulutsidwa wosaweruzikayo, amene Ambuye Yesu adzamthera ndi mzimu wa pakamwa pake, nadzamuononga ndi maonekedwe a kudza kwake;


Chifukwa chake lapa; ukapanda kutero ndidza kwa iwe posachedwa, ndipo ndidzachita nao nkhondo ndi lupanga la m'kamwa mwanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa