Yobu 4:9 - Buku Lopatulika9 Atayika ndi mpweya wa Mulungu, nathedwa ndi mpumo wa mkwiyo wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Atayika ndi mpweya wa Mulungu, nathedwa ndi mpumo wa mkwiyo wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Monga momwe mphepo ya mkuntho imasakazira zinthu, Mulungu amaŵaononga ndi mkwiyo wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iwo amaphedwa ndi mpweya wa Mulungu; amawonongeka ndi mpweya waukali wa mkwiyo wake. Onani mutuwo |