Yobu 4:7 - Buku Lopatulika7 Takumbukira tsopano, watayika ndani wosapalamula konse? Kapena oongoka mtima alikhidwa kuti? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Takumbukira tsopano, watayika ndani wosapalamula konse? Kapena oongoka mtima alikhidwa kuti? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Ganiza bwino tsopano: Kodi alipo munthu wosachimwa amene adaonongekapo nkale lonse? Nanga nkuti kumene udaona anthu olungama ataphedwa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Ganiza bwino tsopano: Kodi munthu wosalakwa anawonongekapo nʼkale lonse? Nʼkuti kumene munthu wolungama mtima anaphedwa? Onani mutuwo |