Yobu 4:4 - Buku Lopatulika4 Mau ako anachirikiza iye amene akadagwa, walimbitsanso maondo otewa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mau ako anachirikiza iye amene akadagwa, walimbitsanso maondo otewa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mau ako adathandiza munthu wofuna kugwa, adachirikiza munthu wotha mphamvu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mawu ako analimbitsa anthu ofuna kugwa; unachirikiza anthu wotha mphamvu. Onani mutuwo |