Yobu 4:3 - Buku Lopatulika3 Taona iwe walangiza aunyinji, walimbitsa manja a ofooka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Taona iwe walangiza aunyinji, walimbitsa manja a ofooka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Taona, iwe waphunzitsa anthu ambiri, walimbitsa mtima anthu ofooka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Taganiza momwe iwe walangizira anthu ambiri, momwe walimbitsira anthu ofowoka. Onani mutuwo |