Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 4:2 - Buku Lopatulika

2 Munthu akayesa kunena nawe mau, kodi udzamva nao chisoni? Koma akhoza ndani kudziletsa kunena?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Munthu akayesa kunena nawe mau, kodi udzamva nao chisoni? Koma akhoza ndani kudziletsa kunena?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 “Iwe Yobe, kodi wina atakuyankha, ndiye kuti wakulakwira? Ah, koma ine ndekha sindingathe kukhala chete.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 “Ngati wina atakuyankha, kodi ungakhumudwe? Koma ndani angakhale chete wosayankhula?

Onani mutuwo Koperani




Yobu 4:2
7 Mawu Ofanana  

Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati,


Ndipo ngati nditi, Sindidzamtchula Iye, sindidzanenanso m'dzina lake, pamenepo m'mtima mwanga muli ngati moto wotentha wotsekedwa m'mafupa anga, ndipo ndalema ndi kupirira, sindingathe kupiriranso.


Chifukwa chake ndadzala ndi ukali wa Yehova; ndalema ndi kudzikaniza; tsanulirani pa ana a pabwalo, ndi pa misonkhano ya anyamata, pakuti ngakhale mwamuna ndi mkazi wake adzatengedwa, okalamba ndi iye amene achuluka masiku ake.


pakuti sitingathe ife kuleka kulankhula zimene tinaziona ndi kuzimva.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa