Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 4:10 - Buku Lopatulika

10 Kubangula kwa mkango, ndi kulira kwa mkango waukali kwaletsedwa, ndi mano a misona ya mkango athyoledwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Kubangula kwa mkango, ndi kulira kwa mkango waukali kwaletsedwa, ndi mano a misona ya mkango athyoledwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Anthu oipa amakhuluma ngati mkango, koma Mulungu amaŵathyola mano.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Mikango imabangula ndi kulira, komabe mano a mikango yamphamvu amathyoledwa.

Onani mutuwo Koperani




Yobu 4:10
7 Mawu Ofanana  

Ndipo ndinathyola nsagwada ya wosalungama, ndi kukwatula chogwidwa kumano kwake.


Apulumutsa aumphawi kulupanga la kukamwa kwao, ndi kudzanja la wamphamvu.


Ukani Yehova; ndipulumutseni, Mulungu wanga! Pakuti mwapanda adani anga onse patsaya; mwawathyola mano oipawo.


Moyo wanga uli pakati pa mikango; ndigona pakati pa oyaka moto, ndiwo ana a anthu amene mano ao ali nthungo ndi mivi, ndipo lilime lao ndilo lupanga lakuthwa.


Thyolani mano ao m'kamwa mwao, Mulungu, zulani zitsakano za misona ya mkango, Yehova.


Apitetu ngati madzi oyenda; popiringidza mivi yake ikhale yodukaduka.


Pali mbadwo mano ao akunga malupanga, zibwano zao zikunga mipeni; kuti adye osauka kuwachotsa kudziko, ndi aumphawi kuwachotsa mwa anthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa