Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 4:1 - Buku Lopatulika

1 Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Tsono Elifazi wa ku Temani adati,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yobu 4:1
10 Mawu Ofanana  

Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati,


Atamva tsono mabwenzi atatu a Yobu za choipa ichi chonse chidamgwera, anadza, yense kuchokera kwao, Elifazi wa ku Temani, ndi Bilidadi Msuki, ndi Zofari wa ku Naama, napangana kudzafika kumlirira ndi kumsangalatsa.


Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati,


Wosakhazikika, ndi wosakhala chete, ndi wosapumula ine, koma mavuto anandidzera.


Munthu akayesa kunena nawe mau, kodi udzamva nao chisoni? Koma akhoza ndani kudziletsa kunena?


Namuka Elifazi wa ku Temani, ndi Bilidadi Msuki, ndi Zofari wa ku Naama, nachita monga Yehova adawauza; ndipo Yehova anavomereza Yobu.


Koma Yobu anayankha, nati,


Pamenepo anayankha Bilidadi Msuki, nati,


Za Edomu. Yehova wa makamu atero: Kodi mu Temani mulibenso nzeru? Kodi uphungu wawathera akuchenjera? Kodi nseru zao zatha psiti?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa