Yobu 39:3 - Buku Lopatulika3 Zithuntha, ziswa, zitaya zowawa zao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Zithuntha, ziswa, zitaya zowawa zao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kodi ukuidziŵa nthaŵi imene zidzakhala tsonga nkuswa ana, kenaka nkutayiza? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Zimakhala tsonga ndi kuswa ana awo; pamenepo ululu wobereka nʼkutha. Onani mutuwo |