Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 39:2 - Buku Lopatulika

2 Ukhoza kodi kuwerenga miyezi yakuzipitira, kapena udziwa nyengo yoti ziswane?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ukhoza kodi kuwerenga miyezi yakuzipitira, kapena udziwa nyengo yoti ziswane?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Kodi ungathe kuŵerenga miyezi imene zimakhala ndi bele? Kodi nthaŵi imene nyamazi zimaswa iwe umaidziŵa?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Kodi umawerenga miyezi imene zimakhala ndi bere? Kodi nthawi imene zimaswana iwe umayidziwa?

Onani mutuwo Koperani




Yobu 39:2
3 Mawu Ofanana  

Kodi udziwa nyengo yakuswana zinkhoma? Kodi wapenyerera pakuswa mbawala?


Zithuntha, ziswa, zitaya zowawa zao.


mbidzi yozolowera m'chipululu, yopumira mphepo pakufuna pake; pokomana nayo ndani adzaibweza? Onse amene aifuna sadzadzilemetsa; adzaipeza m'mwezi wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa