Yobu 38:3 - Buku Lopatulika3 Udzimangire m'chuuno tsono ngati mwamuna; ndikufunsa, undidziwitse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Udzimangire m'chuuno tsono ngati mwamuna; ndikufunsa, undidziwitse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Onetsa chamuna, ndidzakufunsa, ndipo undiyankhe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Onetsa chamuna; ndikufunsa ndipo undiyankhe. Onani mutuwo |