Yobu 32:5 - Buku Lopatulika5 Koma pakuona Elihu kuti anthu atatuwa anasowa poyankha pakamwa pao anapsa mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma pakuona Elihu kuti anthu atatuwa anasowa poyankha pakamwa pao anapsa mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsono ataona kuti anthu atatuwo sadamuyankhe Yobe moyenera, adapsa mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma Elihu ataona kuti anthu atatuwo analibe mawu oti ayankhulenso, iye anapsa mtima. Onani mutuwo |