Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 32:5 - Buku Lopatulika

5 Koma pakuona Elihu kuti anthu atatuwa anasowa poyankha pakamwa pao anapsa mtima.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Koma pakuona Elihu kuti anthu atatuwa anasowa poyankha pakamwa pao anapsa mtima.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Tsono ataona kuti anthu atatuwo sadamuyankhe Yobe moyenera, adapsa mtima.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Koma Elihu ataona kuti anthu atatuwo analibe mawu oti ayankhulenso, iye anapsa mtima.

Onani mutuwo Koperani




Yobu 32:5
4 Mawu Ofanana  

Ndipo adapsa mtima Elihu mwana wa Barakele wa ku Buzi, wa chibale cha Ramu, adapsa mtima pa Yobu; pakuti anadziyesera yekha wolungama, wosati Mulungu.


Ndipo Elihu analindira kulankhula ndi Yobu, popeza akulu misinkhu ndi iwowa.


Ndipo Elihu mwana wa Barakele wa ku Buzi anayankha, nati, Ine ndine mnyamata, inu ndinu okalamba; chifukwa chake ndinadziletsa, ndi kuopa kukuonetsani monga umo ndayesera ine.


Ndipo kunali, pamene anayandikiza chigono, anaona mwanawang'ombeyo ndi kuvinako; ndipo Mose anapsa mtima, nataya magome ali m'manja mwake, nawaswa m'tsinde mwa phiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa