Yobu 32:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Elihu analindira kulankhula ndi Yobu, popeza akulu misinkhu ndi iwowa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Elihu analindira kulankhula ndi Yobu, popeza akulu misinkhu ndi iwowa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Koma Elihu adadikira kuti alankhule ndi Yobe, chifukwa choti abwenziwo anali akuluakulu kupambana iyeyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tsono Elihu anadikira kuti ayankhule ndi Yobu chifukwa choti abwenziwo anali akuluakulu kupambana iyeyo. Onani mutuwo |