Yobu 32:3 - Buku Lopatulika3 Adapsa mtima pa mabwenzi ake atatu omwe, pakuti anasowa pomyankha; koma anamtsutsa Yobu kuti ali woipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Adapsa mtima pa mabwenzi ake atatu omwe, pakuti anasowa pomyankha; koma anamtsutsa Yobu kuti ali woipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Adapseranso mtima abwenzi ake atatu aja, chifukwa choti sadathe kuyankha, ngakhale iwo omwe adaapeza kuti Yobeyo ndi wolakwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Anapseranso mtima abwenzi ake atatu aja chifukwa sanapeze njira yomutsutsira Yobu, ngakhale iwo anamupeza kuti anali wolakwa. Onani mutuwo |