Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 32:3 - Buku Lopatulika

3 Adapsa mtima pa mabwenzi ake atatu omwe, pakuti anasowa pomyankha; koma anamtsutsa Yobu kuti ali woipa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Adapsa mtima pa mabwenzi ake atatu omwe, pakuti anasowa pomyankha; koma anamtsutsa Yobu kuti ali woipa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Adapseranso mtima abwenzi ake atatu aja, chifukwa choti sadathe kuyankha, ngakhale iwo omwe adaapeza kuti Yobeyo ndi wolakwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Anapseranso mtima abwenzi ake atatu aja chifukwa sanapeze njira yomutsutsira Yobu, ngakhale iwo anamupeza kuti anali wolakwa.

Onani mutuwo Koperani




Yobu 32:3
12 Mawu Ofanana  

Pakuti msonkhano wa onyoza Mulungu udzakhala chumba, ndi moto udzapsereza mahema a olandira chokometsera mlandu.


Ndipo ngati si kutero, anditsutsa ndani kuti ndili wabodza, ndi kuyesa mau anga opanda pake?


Pamenepo amuna atatuwa analeka kumyankha Yobu; pakuti anali wolungama pamaso pake pa iye mwini.


Ndipo adapsa mtima Elihu mwana wa Barakele wa ku Buzi, wa chibale cha Ramu, adapsa mtima pa Yobu; pakuti anadziyesera yekha wolungama, wosati Mulungu.


Ndipo Elihu analindira kulankhula ndi Yobu, popeza akulu misinkhu ndi iwowa.


Kunali tsono atanena Yehova mau awa kwa Yobu, Yehova anati kwa Elifazi wa ku Temani, Mkwiyo wanga wakuyakira iwe ndi mabwenzi ako awiri, pakuti simunandinenere choyenera monga ananena mtumiki wanga Yobu.


ukakhala woyera ndi woongoka mtima, zoonadi adzakugalamukira tsopano, ndi kupindulitsa pokhala pako polungama.


Ndipo sangathe kukutsimikizirani zimene andinenera ine tsopano.


Pakuti tapeza munthuyu ali ngati mliri, ndi woutsa mapanduko kwa Ayuda onse m'dziko lonse lokhalamo anthu, ndi mtsogoleri wa mpanduko wa Anazarene;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa